Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 8:3, 4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Ndikayangʼana kumwamba, ntchito ya zala zanu,

      Mwezi ndi nyenyezi zimene munapanga,+

       4 Ndimaganiza kuti, munthu ndi ndani kuti muzimuganizira,

      Ndipo mwana wa munthu ndi ndani kuti muzimusamalira?+

  • Yesaya 40:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Pali winawake amene amakhala pamwamba pa dziko lapansi lomwe ndi lozungulira,+

      Ndipo amene amakhala mʼdzikolo ali ngati ziwala.

      Iye anatambasula kumwamba ngati nsalu yopyapyala,

      Ndipo anakufutukula ngati tenti yoti azikhalamo.+

  • Aroma 1:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Kuchokera pamene dziko linalengedwa, makhalidwe a Mulungu osaoneka ndi maso akuonekera bwino. Makhalidwe a Mulungu amenewa,+ ngakhalenso mphamvu zake zosatha+ ndiponso Umulungu wake,+ zikuonekera mʼzinthu zimene anapanga moti anthuwo alibenso chifukwa chomveka chosakhulupirira kuti kuli Mulungu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena