Salimo 8:3, 4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Ndikayangʼana kumwamba, ntchito ya zala zanu,Mwezi ndi nyenyezi zimene munapanga,+ 4 Ndimaganiza kuti, munthu ndi ndani kuti muzimuganizira,Ndipo mwana wa munthu ndi ndani kuti muzimusamalira?+ Yesaya 40:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Pali winawake amene amakhala pamwamba pa dziko lapansi lomwe ndi lozungulira,+Ndipo amene amakhala mʼdzikolo ali ngati ziwala. Iye anatambasula kumwamba ngati nsalu yopyapyala,Ndipo anakufutukula ngati tenti yoti azikhalamo.+ Aroma 1:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Kuchokera pamene dziko linalengedwa, makhalidwe a Mulungu osaoneka ndi maso akuonekera bwino. Makhalidwe a Mulungu amenewa,+ ngakhalenso mphamvu zake zosatha+ ndiponso Umulungu wake,+ zikuonekera mʼzinthu zimene anapanga moti anthuwo alibenso chifukwa chomveka chosakhulupirira kuti kuli Mulungu.
3 Ndikayangʼana kumwamba, ntchito ya zala zanu,Mwezi ndi nyenyezi zimene munapanga,+ 4 Ndimaganiza kuti, munthu ndi ndani kuti muzimuganizira,Ndipo mwana wa munthu ndi ndani kuti muzimusamalira?+
22 Pali winawake amene amakhala pamwamba pa dziko lapansi lomwe ndi lozungulira,+Ndipo amene amakhala mʼdzikolo ali ngati ziwala. Iye anatambasula kumwamba ngati nsalu yopyapyala,Ndipo anakufutukula ngati tenti yoti azikhalamo.+
20 Kuchokera pamene dziko linalengedwa, makhalidwe a Mulungu osaoneka ndi maso akuonekera bwino. Makhalidwe a Mulungu amenewa,+ ngakhalenso mphamvu zake zosatha+ ndiponso Umulungu wake,+ zikuonekera mʼzinthu zimene anapanga moti anthuwo alibenso chifukwa chomveka chosakhulupirira kuti kuli Mulungu.