Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 32:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Ndinu malo anga obisalamo,

      Mudzanditeteza ku mavuto.+

      Mwachititsa kuti ndizunguliridwe ndi anthu amene akufuula mosangalala chifukwa chakuti mwandipulumutsa.+ (Selah)

  • Salimo 57:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 57 Ndikomereni mtima inu Mulungu, ndikomereni mtima,

      Chifukwa ine ndathawira kwa inu.+

      Ndathawira mumthunzi wa mapiko anu mpaka mavuto atadutsa.+

  • Zefaniya 2:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Funafunani Yehova,+ inu nonse ofatsa* apadziko lapansi,

      Amene mumatsatira malamulo ake olungama.*

      Yesetsani kukhala olungama, yesetsani kukhala ofatsa.*

      Mwina mungadzabisike pa tsiku la mkwiyo wa Yehova.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena