Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 11:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Yehova ali mʼkachisi wake wopatulika.+

      Mpando wachifumu wa Yehova uli kumwamba.+

      Maso ake amaona, inde maso ake* amayangʼanitsitsa ana a anthu.+

  • Salimo 14:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Koma kuchokera kumwamba, Yehova amayangʼana ana a anthu,

      Kuti aone ngati pali aliyense wozindikira, ngati pali aliyense amene akufunafuna Yehova.+

  • Miyambo 15:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Maso a Yehova ali paliponse,

      Amaona anthu oipa ndi abwino omwe.+

  • Aheberi 4:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Palibe cholengedwa chimene Mulungu sangathe kuchiona.+ Chifukwa kwa iye zinthu zonse zili poonekera ndipo amatha kuziona bwinobwino moti ifeyo tidzayankha kwa Mulunguyo pa zochita zathu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena