Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 21:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Nʼchifukwa chiyani oipa amakhalabe ndi moyo,+

      Amakalamba komanso amalemera* kwambiri?+

  • Salimo 73:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Chifukwa ndinkachitira nsanje anthu onyada*

      Ndikamaona mtendere wa anthu oipa.+

  • Yeremiya 12:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Inu Yehova, ndikabweretsa dandaulo langa kwa inu,

      Komanso ndikamalankhula ndi inu nkhani zokhudza chilungamo, mumasonyeza kuti ndinu wolungama.+

      Koma nʼchifukwa chiyani anthu oipa, zinthu zikuwayendera bwino,+

      Ndipo nʼchifukwa chiyani anthu amene amachita zachinyengo amakhala opanda nkhawa?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena