Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 13:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndiyeno mʼtsogolo ana anu akadzakufunsani kuti, ‘Kodi zimenezi zikutanthauza chiyani?’ mudzawayankhe kuti, ‘Yehova anatitulutsa ndi dzanja lake lamphamvu mu Iguputo, mʼnyumba ya ukapolo.+

  • Numeri 21:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Nʼchifukwa chake buku la Nkhondo za Yehova limanena za “Vahebi ku Sufa ndi zigwa za Arinoni.*

  • Oweruza 6:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Koma Gidiyoni anayankha kuti: “Pepani mbuyanga, ngati Yehova ali nafe, nʼchifukwa chiyani tikukumana ndi mavuto onsewa?+ Nanga ntchito zake zodabwitsa zimene makolo athu anatiuza zija zili kuti?+ Iwo anatiuza kuti, ‘Yehova ndi amene anatitulutsa ku Iguputo.’+ Koma tsopano Yehova watisiya,+ ndipo watipereka kwa Amidiyani.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena