Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mika 6:6-8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Kodi nditenge chiyani popita kwa Yehova?

      Ndikagwade ndi chiyani kwa Mulungu wakumwamba?

      Kodi ndipite nditatenga nsembe zopsereza zathunthu?

      Ndiponso ana a ngʼombe achaka chimodzi?+

       7 Kodi Yehova adzasangalala ndi masauzande a nkhosa zamphongo?

      Kodi adzakondwera ndi mitsinje ya mafuta masauzande ambirimbiri?+

      Kodi ndipereke mwana wanga wamwamuna woyamba chifukwa cha zolakwa zanga,

      Ndipereke chipatso cha mimba yanga chifukwa cha tchimo langa?+

       8 Iye anakuuza munthu iwe zimene zili zabwino.

      Kodi Yehova akufuna kuti uzichita* chiyani?

      Iye akungofuna kuti uzichita chilungamo,*+ uziona kuti kukhulupirika nʼkofunika,*+

      Ndiponso uziyenda modzichepetsa+ ndi Mulungu wako.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena