22 Tsoka kwa anthu amene amatchuka ndi kumwa vinyo kwambiri,
Komanso kwa anthu amene ndi akatswiri odziwa kusakaniza mowa.+
23 Tsoka kwa anthu amene amaweruza kuti woipa alibe mlandu chifukwa choti alandira chiphuphu,+
Ndiponso kwa amene amalephera kuweruza anthu olungama mwachilungamo.+