Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 9:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Anthu oipa adzapita ku Manda,*

      Anthu a mitundu yonse amene aiwala Mulungu adzapita kumeneko.

  • Yeremiya 2:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Kodi namwali angaiwale zinthu zake zodzikongoletsera?

      Kodi mkwatibwi angaiwale lamba wake wapachifuwa?*

      Komatu anthu anga andiiwala kwa masiku osawerengeka.+

  • Hoseya 4:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Anthu anga adzakhalitsidwa chete* chifukwa cha kusadziwa.

      Popeza iwo akana kundidziwa,+

      Inenso ndidzawakana kuti asamanditumikire ngati wansembe wanga.

      Komanso chifukwa chakuti iwo aiwala lamulo* la ine Mulungu wawo,+

      Inenso ndidzaiwala ana awo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena