Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Esitere 6:11, 12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Choncho Hamani anatenga chovala ndi hatchi, ndipo anaveka Moredikayi+ chovalacho. Kenako anamʼkweza pahatchiyo nʼkumuyendetsa mʼbwalo la mzinda, akufuula patsogolo pake kuti: “Izi ndi zimene timachitira munthu amene mfumu yafuna kumʼpatsa ulemu!” 12 Kenako, Moredikayi anabwerera kugeti la mfumu. Koma Hamani anapita kunyumba kwake mofulumira, akulira ndiponso ataphimba kumutu.

  • Miyambo 12:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Munthu amatamandidwa chifukwa cholankhula zinthu zanzeru,+

      Koma amene ali ndi mtima wopotoka adzanyozedwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena