Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 26:13-15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Waulesi amanena kuti: “Mumsewu muli mkango wamphamvu,

      Mʼbwalo la mzinda mukuyendayenda mkango.”+

      14 Mofanana ndi chitseko chimene chimangozungulira pamene anachimangirira,

      Waulesi nayenso amangotembenukatembenuka pabedi pake.+

      15 Munthu waulesi amapisa dzanja lake mʼmbale ya chakudya,

      Koma amalephera kulibweretsa pakamwa pake chifukwa chotopa kwambiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena