Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 17:45, 46
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 Davide anayankha Mfilisitiyo kuti: “Iwe ukubwera kudzamenyana ndi ine ndi lupanga, mkondo ndi nthungo,+ koma ine ndikubwera kudzamenyana nawe mʼdzina la Yehova wa magulu ankhondo akumwamba,+ Mulungu wa asilikali a Isiraeli, amene iweyo wamunyoza.+ 46 Lero Yehova akupereka mʼmanja mwanga,+ ndipo ndikupha nʼkukudula mutu. Lero ndipereka mitembo ya asilikali amʼmisasa ya Afilisiti kwa mbalame zamumlengalenga ndi kwa zilombo zakutchire. Anthu onse apadziko lapansi adzadziwa kuti Aisiraeli ali ndi Mulungu.+

  • Salimo 20:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Yehova akuyankheni pa tsiku la mavuto.

      Dzina la Mulungu wa Yakobo likutetezeni.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena