Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 3:7-9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Tsopano Yehova Mulungu wanga, mwandiika ine mtumiki wanu kukhala mfumu mʼmalo mwa Davide bambo anga, ngakhale kuti ndine wamngʼono ndipo sindikudziwa zambiri.+ 8 Ine mtumiki wanu ndili pakati pa anthu anu amene mwawasankha,+ anthu ambirimbiri osatheka kuwawerenga. 9 Mundipatse ine mtumiki wanu mtima womvera kuti ndiweruze anthu anu+ komanso ndizitha kusiyanitsa zabwino ndi zoipa.+ Ndani angathe kuweruza anthu anu ambirimbiriwa?”*

  • Miyambo 9:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Pereka malangizo kwa munthu wanzeru ndipo adzawonjezera nzeru zake.+

      Phunzitsa munthu wolungama ndipo adzapitiriza kuphunzira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena