Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 37:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Onani munthu wosalakwa,*

      Ndipo yangʼanitsitsani munthu wolungama,+

      Chifukwa tsogolo la munthu ameneyo lidzakhala lamtendere.+

  • Miyambo 16:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Anthu owongoka mtima amapewa kuchita zinthu zoipa.

      Aliyense amene amateteza njira yake, amasunga moyo wake.+

  • 1 Petulo 1:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Popeza mwadziyeretsa pokhala omvera choonadi cha mʼMawu a Mulungu ndipo tsopano mumakonda abale mopanda chinyengo,+ muzikondana kwambiri kuchokera mumtima.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena