Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 141:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Inu Yehova, ikani mlonda pakamwa panga.

      Ikani woti azilondera patsogolo pa milomo yanga.+

  • Miyambo 10:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Mawu akachuluka sipalephera kukhala zolakwika,+

      Koma amene amalamulira milomo yake amachita zinthu mwanzeru.+

  • Mlaliki 10:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ngakhale mʼmaganizo mwako,* usatemberere* mfumu+ ndipo usatemberere munthu wolemera kuchipinda kwako. Chifukwa mbalame* ikhoza kutenga mawu ako* kapena cholengedwa chokhala ndi mapiko chikhoza kukaulula zimene wanenazo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena