Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 11:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Pakakhala popanda malangizo anzeru, anthu amagwa.

      Koma zinthu zimayenda bwino* ngati pali alangizi* ambiri.+

  • Miyambo 13:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kudzikuza kumangoyambitsa mikangano basi,+

      Koma anthu amene amapempha malangizo* amakhala ndi nzeru.+

  • Miyambo 15:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Mapulani sakwaniritsidwa ngati anthu sakambirana,*

      Koma alangizi akachuluka zinthu zimayenda bwino.+

  • Machitidwe 15:5, 6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Koma okhulupirira ena, amene kale anali mʼgulu lampatuko la Afarisi, anaimirira mʼmipando yawo nʼkunena kuti: “Mʼpofunika kuwadula komanso kuwalamula kuti azisunga Chilamulo cha Mose.”+

      6 Choncho atumwi ndi akulu anasonkhana kuti akambirane za nkhani imeneyi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena