Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 31:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Kodi ndinayamba ndasangalalapo chifukwa cha kuwonongedwa kwa mdani wanga,+

      Kapena kunyadira chifukwa chakuti zoipa zamuchitikira?

  • Miyambo 17:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Wonyoza munthu wosauka amanyoza amene anamupanga.+

      Ndipo amene amasangalala ndi tsoka la wina sadzalephera kulangidwa.+

  • Miyambo 25:21, 22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ngati mdani wako* ali ndi njala, umʼpatse chakudya.

      Ngati ali ndi ludzu, umʼpatse madzi akumwa,+

      22 Ukachita zimenezi ndiye kuti ukumuunjikira makala amoto pamutu pake,*+

      Ndipo Yehova adzakupatsa mphoto.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena