Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 18:8, 9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Sauli anakwiya kwambiri+ ndipo nyimbo imeneyi inkamunyasa, moti anayamba kuganiza kuti: “Akutamanda Davide ponena kuti wapha masauzande ambirimbiri, koma ine akunena kuti ndapha masauzande okha. Ndiye kuti kwatsala nʼkumupatsa ufumuwutu basi!”+ 9 Kuyambira tsiku limenelo, Sauli anayamba kuyangʼana Davide ndi diso loipa.

  • Yakobo 3:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Chifukwa pamene pali nsanje ndi mtima wokonda mikangano,* pamakhalanso chisokonezo ndi zoipa zamtundu uliwonse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena