Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 23:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Musamalandire chiphuphu chifukwa chiphuphu chimachititsa khungu anthu amene amaona bwinobwino, ndipo chingapotoze mawu a anthu olungama.+

  • Deuteronomo 16:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Musamakhotetse chilungamo,+ musamakondere+ kapena kulandira chiphuphu, chifukwa chiphuphu chimachititsa khungu maso a anthu anzeru+ komanso kupotoza mawu a anthu olungama.

  • 1 Samueli 8:1-3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Samueli atakalamba, anaika ana ake aamuna kuti akhale oweruza mu Isiraeli. 2 Mwana wake woyamba anali Yoweli, ndipo wachiwiri anali Abiya.+ Iwo anali oweruza ku Beere-seba. 3 Ana akewa sanatsatire chitsanzo chake. Iwo ankakonda kupeza phindu mwachinyengo,+ kulandira ziphuphu+ ndiponso kupotoza chilungamo.+

  • Miyambo 17:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Munthu woipa amalandira chiphuphu mobisa,

      Kuti akhotetse chilungamo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena