Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mlaliki 1:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndinatsimikiza mumtima mwanga kuti ndiphunzire ndi kufufuza mwanzeru+ zonse zimene zachitidwa padziko lapansi.+ Ndinafufuza ntchito yotopetsa kwambiri imene Mulungu wapatsa ana a anthu kuti azigwira.

  • Mlaliki 7:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Mumtima mwanga ndinasankha kuti ndidziwe, ndifufuze ndiponso ndifunefune nzeru komanso chifukwa chake zinthu zinazake zimachitika. Ndinafunanso kumvetsa kuti uchitsiru ndi woipa bwanji komanso makhalidwe opusa a anthu amene amachita zinthu ngati amisala.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena