-
1 Mafumu 4:25Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
25 Ayuda ndi Aisiraeli ankakhala mwamtendere. Aliyense ankakhala pansi pa mtengo wake wa mpesa ndi mtengo wake wa mkuyu, kuchokera ku Dani mpaka ku Beere-seba, masiku onse a Solomo.
-