Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 71:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Inu Mulungu, mwandiphunzitsa kuyambira ndili mnyamata,+

      Ndipo mpaka pano ndikupitiriza kulengeza ntchito zanu zodabwitsa.+

  • Salimo 148:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Tamandani Yehova, inu okhala padziko lapansi,

      Inu zamoyo zikuluzikulu zamʼnyanja komanso inu nonse madzi akuya,

  • Salimo 148:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Inu anyamata komanso inu atsikana,*

      Inu achikulire limodzi ndi ana.

  • Luka 2:48, 49
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 48 Makolo akewo atamuona anadabwa kwambiri, ndipo mayi ake anamufunsa kuti: “Mwanawe, nʼchifukwa chiyani wativutitsa chonchi? Ine ndi bambo akowa tinali ndi nkhawa kwambiri ndipo timakufunafuna.” 49 Koma iye anawayankha kuti: “Mumandifunafuna chifukwa chiyani? Kodi simumadziwa kuti ndiyenera kupezeka mʼnyumba ya Atate wanga?”+

  • 2 Timoteyo 3:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kuyambira pamene unali wakhanda,+ wadziwa malemba oyera+ amene angakupatse nzeru zokuthandiza kuti udzapulumuke chifukwa chokhulupirira Khristu Yesu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena