Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 10:14, 15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Golide amene ankabwera kwa Solomo pa chaka, anali wolemera matalente 666,+ 15 osawerengera golide wochokera kwa amalonda oyendayenda, phindu lochokera kwa amalonda komanso golide wochokera kwa mafumu onse a Aluya ndi kwa abwanamkubwa amʼdzikolo.

  • 2 Mbiri 9:13, 14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Golide amene ankabwera kwa Solomo pa chaka, anali wolemera matalente 666,+ 14 osawerengera golide wochokera kwa amalonda oyendayenda ndi amalonda ena, komanso wochokera kwa mafumu onse a Aluya ndi kwa abwanamkubwa amʼdzikolo, amene ankabweretsa golide ndi siliva kwa Solomo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena