Salimo 49:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Aliyense amaona kuti ngakhale anthu anzeru amafa,Munthu wopusa komanso munthu wopanda nzeru, onse amawonongeka,+Ndipo chuma chawo amasiyira anthu ena.+ Mlaliki 1:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Ndinaona ntchito zonse zimene zinachitidwa padziko lapansi pano,Ndipo ndinapeza kuti zonse ndi zachabechabe, zili ngati kuthamangitsa mphepo.+ Mlaliki 2:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Chifukwa munthu wanzeru komanso munthu wopusa,+ onsewa sadzakumbukiridwa mpaka kalekale. Mʼmasiku amene akubwerawa aliyense adzaiwalika. Ndipo kodi wanzeru adzafa bwanji? Adzafa mofanana ndi wopusa.+ 1 Timoteyo 6:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Pajatu sitinabwere ndi kanthu mʼdziko ndipo sitingachokemo ndi kanthu.+
10 Aliyense amaona kuti ngakhale anthu anzeru amafa,Munthu wopusa komanso munthu wopanda nzeru, onse amawonongeka,+Ndipo chuma chawo amasiyira anthu ena.+
14 Ndinaona ntchito zonse zimene zinachitidwa padziko lapansi pano,Ndipo ndinapeza kuti zonse ndi zachabechabe, zili ngati kuthamangitsa mphepo.+
16 Chifukwa munthu wanzeru komanso munthu wopusa,+ onsewa sadzakumbukiridwa mpaka kalekale. Mʼmasiku amene akubwerawa aliyense adzaiwalika. Ndipo kodi wanzeru adzafa bwanji? Adzafa mofanana ndi wopusa.+