Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 41:21, 22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 “Bweretsani kuno mlandu wanu,” akutero Yehova.

      “Fotokozani mfundo zanu,” ikutero Mfumu ya Yakobo.

      22 “Tipatseni umboni ndipo mutiuze zinthu zimene zidzachitike.

      Tiuzeni zokhudza zinthu zakale,*

      Kuti tiziganizire mozama nʼkudziwa tsogolo lake.

      Kapena mutiuze zinthu zimene zikubwera.+

  • Yesaya 44:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Kodi ndi ndani amene angafanane ndi ine?+

      Ayankhe molimba mtima ndi kupereka umboni wake kwa ine.+

      Kuyambira nthawi imene ndinakhazikitsa anthu akalekale,

      Iwo anene zinthu zimene zichitike posachedwapa

      Ndi zimene zidzachitike mʼtsogolo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena