Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 45:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 Izi ndi zimene Yehova akunena kwa wodzozedwa wake, kwa Koresi,+

      Amene wamugwira dzanja lake lamanja+

      Kuti agonjetse mitundu ya anthu pamaso pake,+

      Kuti alande zida zankhondo za mafumu,*

      Kuti amutsegulire zitseko zokhala ziwiriziwiri,

      Kuti mageti adzakhale osatseka. Iye wamuuza kuti:

       2 “Ine ndidzakhala patsogolo pako+

      Ndipo ndidzasalaza zitunda.

      Ndidzaphwanyaphwanya zitseko zakopa,*

      Ndipo ndidzadula zitsulo zotsekera zitseko.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena