8 “Koma iwe Isiraeli, ndiwe mtumiki wanga,+
Iwe Yakobo, amene ndakusankha,+
Mbadwa ya mnzanga Abulahamu.+
-
1 Petulo 2:9
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
9 Koma inu ndi “fuko losankhidwa mwapadera, ansembe achifumu, mtundu woyera+ ndiponso anthu oti adzakhale chuma chapadera.+ Mwasankhidwa kuti mulengeze makhalidwe abwino kwambiri”+ a Mulungu amene anakuitanani kuti muchoke mumdima ndipo anakulandirani mʼkuwala kwake kodabwitsa.+