Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 2:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Yehova wanena kuti:

      “Kodi makolo anu anandipeza ndi vuto lotani+

      Kuti asochere nʼkupita kutali ndi ine,

      Nʼkuyamba kutsatira mafano opanda pake,+ iwonso nʼkukhala anthu opanda pake?+

  • Hoseya 7:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kunyada kwa Aisiraeli kwakhala umboni wowatsutsa,+

      Koma iwo sanabwerere kwa Yehova Mulungu wawo.+

      Ndiponso sanamufunefune ngakhale kuti pali zonsezi.

  • Mika 6:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 “Inu anthu anga, ndakulakwirani chiyani?

      Kodi ndachita chiyani kuti ndikutopetseni?+

      Perekani umboni wonditsutsa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena