Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 66:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Munthu amene akupha ngʼombe yamphongo ali ngati amene akupha munthu.+

      Amene akupereka nsembe ya nkhosa ali ngati amene akuthyola khosi la galu.+

      Munthu amene akupereka mphatso ali ngati amene akupereka magazi a nkhumba.+

      Amene akupereka nsembe yachikumbutso ya lubani+ ali ngati munthu amene akupereka dalitso pogwiritsa ntchito mawu onenerera zamatsenga.*+

      Anthuwo asankha njira zawozawo,

      Ndipo amasangalala ndi zinthu zonyansa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena