Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 29:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ndinu osokoneza zinthu kwambiri!*

      Kodi woumba zinthu ndi dongo angafanane ndi dongolo?+

      Kodi chinthu chimene chinapangidwa, chinganene za amene anachipanga kuti:

      “Iye uja sanandipange”?+

      Komanso kodi chinthu chochita kuumbidwa chinganene za amene anachiumba kuti:

      “Iye uja samvetsa zinthu”?+

  • Yeremiya 18:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 “‘Inu a nyumba ya Isiraeli, kodi sindingakuchiteni zofanana ndi zimene woumba mbiyayu anachita?’ akutero Yehova. ‘Tamverani! Mofanana ndi dongo limene lili mʼmanja mwa woumba mbiya, ndi mmene inunso mulili kwa ine, inu nyumba ya Isiraeli.+

  • Aroma 9:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Munthu iwe, ndiwe ndani kuti uziyankhana ndi Mulungu?+ Kodi chinthu choumbidwa chingauze munthu amene anachiumba kuti, “Unandipangiranji chonchi?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena