Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 43:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ine ndine Yehova.+ Palibenso mpulumutsi wina kupatulapo ine.”+

  • Yesaya 60:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Iwe udzamwa mkaka wa mitundu ya anthu,+

      Ndipo udzayamwa bere la mafumu.+

      Udzadziwadi kuti ine Yehova ndine Mpulumutsi wako,

      Ndiponso kuti Wamphamvu wa Yakobo ndi Wokuwombola.+

  • Tito 1:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Koma pa nthawi yake, anachititsa kuti mawu ake adziwike kudzera mu ntchito yolalikira imene ndinapatsidwa+ mogwirizana ndi lamulo la Mpulumutsi wathu, Mulungu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena