Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 42:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mulungu woona Yehova,

      Amene analenga kumwamba ndiponso Mulungu Wamkulu amene anakutambasula,+

      Amene anapanga dziko lapansi ndi zonse zimene zili mmenemo,+

      Amene amapereka mpweya kwa anthu amene ali mmenemo,+

      Komanso mzimu* kwa anthu amene amayenda padzikolo,+ wanena kuti:

  • Yeremiya 10:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Iye ndi Mulungu amene anapanga dziko lapansi pogwiritsa ntchito mphamvu zake,

      Amene anakhazikitsa dziko lapansi pogwiritsa ntchito nzeru zake.+

      Amenenso anatambasula kumwamba chifukwa cha kuzindikira kwake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena