Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 41:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Kodi ndi ndani amene wapatsa mphamvu winawake kuchokera kotulukira dzuwa,*+

      Amene wamuitana mwachilungamo kuti ayandikire kumapazi ake,*

      Kuti amupatse mitundu ya anthu

      Ndiponso kuti amuchititse kuti agonjetse mafumu?+

      Kodi ndi ndani amene amawasandutsa fumbi pogwiritsa ntchito lupanga lake,

      Ndipo ndi ndani amene amawabalalitsa ngati mapesi ouluzika ndi mphepo pogwiritsa ntchito uta wake?

  • Yesaya 45:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 Izi ndi zimene Yehova akunena kwa wodzozedwa wake, kwa Koresi,+

      Amene wamugwira dzanja lake lamanja+

      Kuti agonjetse mitundu ya anthu pamaso pake,+

      Kuti alande zida zankhondo za mafumu,*

      Kuti amutsegulire zitseko zokhala ziwiriziwiri,

      Kuti mageti adzakhale osatseka. Iye wamuuza kuti:

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena