Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 1:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Ndidzakupatsani chilango,

      Ndidzakuyengani nʼkuchotseratu zonyansa zanu zonse,

      Ndidzachotsa zinthu zonse zimene zikuchititsa kuti musakhale oyera.+

  • Yeremiya 9:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Choncho, Yehova wa magulu ankhondo akumwamba akuti:

      “Ine ndidzawayenga komanso kuwayesa,+

      Nanga mwana wamkazi wa anthu anga ndingamuchitirenso chiyani?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena