Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 44:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Yehova, Mfumu ya Isiraeli,+ amene anawawombola,+

      Yehova wa magulu ankhondo akumwamba, wanena kuti:

      ‘Ine ndine woyamba ndi womaliza.+

      Ndipo palibenso Mulungu wina kupatulapo ine.+

  • Chivumbulutso 1:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “Ine ndine Alefa ndi Omega,”*+ akutero Yehova* Mulungu, “Iye amene alipo, amene analipo, ndi amene akubwera, Wamphamvuyonse.”+

  • Chivumbulutso 22:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ine ndine Alefa ndi Omega,*+ woyamba ndi wotsiriza, chiyambi ndi mapeto.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena