Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Chivumbulutso 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Komanso kuchokera kwa Yesu Khristu, “Mboni Yokhulupirika,”+ “woyamba kubadwa kuchokera kwa akufa”+ ndiponso “Wolamulira mafumu a dziko lapansi.”+

      Kwa iye amene amatikonda+ komanso amene anatimasula ku machimo athu pogwiritsa ntchito magazi ake,+

  • Chivumbulutso 3:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kwa mngelo wa mpingo wa ku Laodikaya,+ lemba kuti: Izi ndi zimene Ame+ akunena, yemwe ndi mboni+ yokhulupirika komanso yoona,+ woyamba wa chilengedwe cha Mulungu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena