-
Yesaya 44:23Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
23 Fuulani mosangalala kumwamba inu,
Chifukwa Yehova wachita zimenezi.
Fuulani posonyeza kupambana, inu malo otsika kwambiri a dziko lapansi.
Mapiri inu, fuulani mosangalala,+
Iwe nkhalango ndi inu mitengo yonse imene ili mmenemo,
Chifukwa Yehova wawombola Yakobo,
Ndipo wasonyeza kukongola kwake pa Isiraeli.”+
-