Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 6:13, 14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 “Chifukwa aliyense kuyambira wamngʼono mpaka wamkulu, akupeza phindu mwachinyengo.+

      Kuyambira mneneri mpaka wansembe, aliyense akuchita zachinyengo.+

      14 Iwo akuyesa kuchiritsa mwachinyengo kuwonongeka kwa anthu anga* ponena kuti,

      ‘Kuli mtendere! Kuli mtendere!’

      Pamene kulibe mtendere.+

  • Ezekieli 13:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Aneneri a mu Isiraeli adzakhala atawonongedwa. Aneneri amenewa ndi omwe akulosera zokhudza Yerusalemu nʼkumaona masomphenya oti mumzindawo muli mtendere, pamene mulibe mtendere,”’+ akutero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena