Ezekieli 16:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Unamanga malo ako okwerawo pamalo oonekera bwino kwambiri mumsewu uliwonse ndipo kukongola kwako unakusandutsa chinthu chonyansa podzipereka kwa munthu* aliyense wodutsa+ ndipo unachulukitsa zochita zako zauhulezo.+ Ezekieli 16:33 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 33 Anthu amapereka mphatso kwa mahule onse,+ koma iweyo ndi amene wapereka mphatso kwa zibwenzi zako zonse.+ Umawapatsa ziphuphu kuti abwere kwa iwe kuchokera kumalo onse ozungulira kuti adzachite nawe zauhule.+ Ezekieli 23:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Oholiba atapitiriza kuchita uhule mopanda manyazi komanso kudzivula,+ ine ndinamusiya chifukwa chonyansidwa naye, ngati mmene ndinasiyira mchemwali wake chifukwa chonyansidwa naye.+
25 Unamanga malo ako okwerawo pamalo oonekera bwino kwambiri mumsewu uliwonse ndipo kukongola kwako unakusandutsa chinthu chonyansa podzipereka kwa munthu* aliyense wodutsa+ ndipo unachulukitsa zochita zako zauhulezo.+
33 Anthu amapereka mphatso kwa mahule onse,+ koma iweyo ndi amene wapereka mphatso kwa zibwenzi zako zonse.+ Umawapatsa ziphuphu kuti abwere kwa iwe kuchokera kumalo onse ozungulira kuti adzachite nawe zauhule.+
18 Oholiba atapitiriza kuchita uhule mopanda manyazi komanso kudzivula,+ ine ndinamusiya chifukwa chonyansidwa naye, ngati mmene ndinasiyira mchemwali wake chifukwa chonyansidwa naye.+