Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 42:24, 25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Ndi ndani wachititsa kuti Yakobo alandidwe katundu wake

      Ndiponso kupereka Isiraeli kwa anthu olanda?

      Kodi si Yehova amene iwo amuchimwira?

      Iwo anakana kuyenda mʼnjira zake,

      Ndipo sanamvere malamulo* ake.+

      25 Choncho Mulungu anapitiriza kuwakhuthulira ukali ndi mkwiyo wake,

      Anawabweretsera nkhondo yoopsa.+

      Moto unapsereza chilichonse chimene anali nacho, koma iwo sanalabadire.+

      Motowo unapitiriza kuwawotcha koma iwo sizinawakhudze.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena