Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 61:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Inuyo mudzatchedwa ansembe a Yehova.+

      Anthu adzakutchulani kuti atumiki a Mulungu wathu.

      Mudzadya zinthu zochokera kumitundu ya anthu+

      Ndiponso mudzadzitamandira chifukwa cha ulemerero umene* mudzapeze kuchokera kwa iwo.

  • Hagai 2:7, 8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 ‘Ndigwedeza mitundu yonse ya anthu, ndipo zinthu zamtengo wapatali zochokera ku mitundu yonse ya anthu zidzalowa mʼnyumba imeneyi.+ Ndipo ndidzadzaza nyumbayi ndi ulemerero,’+ watero Yehova wa magulu ankhondo akumwamba.

      8 ‘Siliva ndi wanga, golidenso ndi wanga,’ watero Yehova wa magulu ankhondo akumwamba.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena