-
Yesaya 60:4Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
4 Kweza maso ako uone zonse zimene zikuchitika mokuzungulira.
Onse asonkhanitsidwa pamodzi. Akubwera kwa iwe.
-
-
Yesaya 66:20Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
20 Adzabweretsa abale anu onse kuchokera ku mitundu yonse+ ngati mphatso kwa Yehova. Adzawabweretsa atakwera mahatchi, ngolo, ngolo zotseka pamwamba, nyulu* ndi ngamila zothamanga, mpaka kukafika kuphiri langa loyera, ku Yerusalemu. Adzachita zimenezi ngati mmene Aisiraeli amabweretsera mphatso mʼnyumba ya Yehova, ataiika mʼchiwiya choyera,” akutero Yehova.
-