Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 36:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Inu ndinu kasupe wa moyo.+

      Chifukwa cha kuwala kochokera kwa inu, timaona kuwala.+

  • Yesaya 60:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 60 “Imirira mkazi iwe!+ Onetsa kuwala kwako, chifukwa kuwala kwako kwafika.

      Ulemerero wa Yehova wakuunikira.+

  • Chivumbulutso 21:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Mzindawo sunafunikirenso kuwala kwa dzuwa kapena kwa mwezi, chifukwa kuwala kwa ulemerero wa Mulungu kunkaunikira mzindawo+ ndipo Mwanawankhosa ndi amene anali nyale yake.+

  • Chivumbulutso 22:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Komanso, usiku sudzakhalakonso+ ndipo sadzafunikiranso kuwala kwa nyale kapena kwa dzuwa, chifukwa Yehova* Mulungu adzawaunikira.+ Ndipo iwo adzalamulira monga mafumu mpaka kalekale.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena