Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 52:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 52 Dzuka! Dzuka! Vala mphamvu+ iwe Ziyoni.+

      Vala zovala zako zokongola+ iwe Yerusalemu, mzinda woyera.

      Chifukwa munthu wosadulidwa ndi wodetsedwa sadzabweranso mwa iwe.+

  • Chivumbulutso 21:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndinaonanso mzinda woyera, Yerusalemu Watsopano, ukutsika kuchokera kumwamba kwa Mulungu+ ndipo unali utakonzedwa ngati mkwatibwi amene wavala zokongola kuti akalandire mwamuna wake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena