Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 137:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Inu Yehova, kumbukirani

      Zimene Aedomu ananena pa tsiku limene Yerusalemu anawonongedwa.

      Iwo anati: “Gwetsani mzindawo! Ugwetseni mpaka pamaziko ake!”+

  • Yesaya 34:5, 6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 “Chifukwa lupanga langa lidzakhala magazi okhaokha kumwambako.+

      Lupangalo lidzatsikira pa Edomu kuti lipereke chiweruzo,+

      Lidzatsikira pa anthu amene ndikufuna kuwawononga.

       6 Yehova ali ndi lupanga. Lupangalo lidzakhala magazi okhaokha.

      Lidzakhala mafuta okhaokha,+

      Lidzakhala ndi magazi a nkhosa zamphongo zingʼonozingʼono komanso a mbuzi,

      Lidzakhala ndi mafuta a impso za nkhosa zamphongo.

      Chifukwa Yehova adzapereka nsembe ku Bozira,

      Adzapha nyama zambiri mʼdziko la Edomu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena