Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 36:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Inatentha nyumba ya Mulungu woona,+ kugwetsa mpanda wa Yerusalemu,+ kutentha nyumba zonse zokhala ndi mipanda yolimba kwambiri ndiponso zinthu zonse zamtengo wapatali.+

  • Yesaya 64:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Nyumba yathu yoyera* ndiponso yaulemerero,*

      Imene makolo athu ankakutamandiranimo,

      Yawotchedwa ndi moto,+

      Ndipo zinthu zathu zonse zimene tinkaziona kuti ndi zamtengo wapatali zasanduka mabwinja

  • Maliro 1:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mdani wamulanda zinthu zake zonse zamtengo wapatali.+

      Yerusalemu waona anthu a mitundu ina akulowa mʼmalo ake opatulika,+

      Mitundu imene munalamula kuti isamalowe mumpingo wanu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena