Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 59:7, 8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Mapazi awo amathamangira kukachita zoipa,

      Ndipo amafulumira kukhetsa magazi a anthu osalakwa.+

      Maganizo awo ndi maganizo oipa.

      Zonse zimene amachita zimakhala zowononga ndiponso zobweretsa mavuto.+

       8 Njira ya mtendere sakuidziwa,

      Ndipo mʼnjira zawo mulibe chilungamo.+

      Misewu yawo aikhotetsakhotetsa.

      Palibe munthu aliyense woyenda mmenemo amene adzadziwe mtendere.+

  • Yeremiya 35:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ndinkakutumizirani mobwerezabwereza*+ atumiki anga onse omwe anali aneneri. Ndinkawauza uthenga wakuti, ‘Chonde bwererani ndipo aliyense asiye njira zake zoipa.+ Muzichita zinthu zabwino. Musatsatire milungu ina nʼkumaitumikira. Mukatero mudzapitiriza kukhala mʼdziko limene ndinapatsa inuyo ndi makolo anu.’+ Koma inu simunatchere khutu kapena kundimvera.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena