Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 17:16, 17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Anasiya malamulo onse a Yehova Mulungu wawo nʼkupanga zifaniziro ziwiri zachitsulo za ana a ngʼombe+ komanso mzati wopatulika.*+ Anayamba kugwadira gulu lonse la zinthu zakuthambo+ ndiponso kulambira Baala.+ 17 Komanso iwo ankawotcha* pamoto ana awo aamuna ndi aakazi,+ kulosera+ ndiponso kuwombeza. Anatsimikiza mtima kuchita zoipa pamaso pa Yehova nʼcholinga chomukwiyitsa.

  • Yeremiya 32:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Akasidi amene akumenyana ndi anthu amumzindawu adzabwera nʼkuyatsa mzindawu moti udzapseratu.+ Adzawotchanso nyumba zimene pamadenga ake anthu ankaperekerapo nsembe kwa Baala komanso nsembe zachakumwa kwa milungu ina kuti andikhumudwitse.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena