Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 62:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Sudzatchedwanso mkazi wosiyidwa,+

      Ndipo dziko lako silidzatchedwanso labwinja.+

      Koma dzina lako lidzakhala Ndimakondwera Naye,+

      Ndipo dziko lako lidzatchedwa Mkazi Wokwatiwa.

      Chifukwa Yehova adzasangalala nawe,

      Ndipo dziko lako lidzakhala ngati mkazi wokwatiwa.

  • Yeremiya 32:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Ndidzasangalala nawo ndipo ndidzawachitira zabwino.+ Ndidzawachititsa kuti azikhala mʼdziko lino+ mpaka kalekale. Ndidzachita zimenezi ndi mtima wanga wonse komanso moyo wanga wonse.’”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena