Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 30:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Hezekiya anatumiza uthenga kwa Aisiraeli+ ndi Ayuda onse ndipo analembera makalata anthu a ku Efuraimu ndi ku Manase+ kuti abwere kunyumba ya Yehova ku Yerusalemu kudzachitira Pasika Yehova Mulungu wa Isiraeli.+

  • 2 Mbiri 30:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Choncho asilikali othamangawo anapita mʼmizinda yonse mʼdera la Efuraimu ndi Manase+ mpaka ku Zebuloni. Koma anthuwo ankangowanyoza ndiponso kuwaseka.+

  • Yeremiya 31:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Chifukwa tsiku lidzafika limene alonda amene ali mʼmapiri a Efuraimu adzafuula kuti:

      ‘Nyamukani, tiyeni tipite ku Ziyoni kwa Yehova Mulungu wathu.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena