Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 3:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Mʼmasiku amenewo nyumba ya Yuda idzayenda pamodzi ndi nyumba ya Isiraeli.+ Onse pamodzi adzabwera kuchokera mʼdziko lakumpoto nʼkulowa mʼdziko limene ndinapereka kwa makolo anu kuti likhale cholowa chawo.+

  • Ezekieli 37:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Koma iwe mwana wa munthu, tenga ndodo nʼkulembapo kuti, ‘Ndodo ya Yuda ndi Aisiraeli amene ali naye.’*+ Kenako utengenso ndodo ina nʼkulembapo kuti, ‘Ndodo ya Yosefe yoimira Efuraimu ndi onse amʼnyumba ya Isiraeli amene ali naye.’*+

  • Ezekieli 37:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Uwauze kuti, ‘Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: “Ine nditenga ndodo ya Yosefe ndi mafuko a Isiraeli amene ali naye. Ndodo imeneyi ili mʼdzanja la Efuraimu. Ndidzaiphatikiza ndi ndodo ya Yuda ndipo idzakhala ndodo imodzi.+ Iwo adzakhala ndodo imodzi mʼdzanja langa.”’

  • Hoseya 1:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ayuda ndi Aisiraeli adzasonkhanitsidwa pamodzi ndipo adzakhala ogwirizana.+ Iwo adzasankha mtsogoleri mmodzi nʼkutuluka mʼdzikolo chifukwa tsiku limeneli lidzakhala lofunika kwambiri kwa Yezereeli.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena